Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 39:22 - Buku Lopatulika

Ndipo anaomba mwinjiro wa efodi, ntchito yoomba ya lamadzi lokha;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anaomba mwinjiro wa efodi, ntchito yoomba ya lamadzi lokha;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adapanga mkanjo wake wa efodi, woombedwa ndi nsalu yobiriŵira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anayipangira efodiyo mkanjo wamtundu wa mtambo, wolukidwa ndi mmisiri waluso.

Onani mutuwo



Eksodo 39:22
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anamanga chapachifuwa pa mphete zake ndi mphete za efodi ndi mkuzi wamadzi, kuti chikhale pa mpango wa efodi, ndi kuti chapachifuwa chisamasuke paefodi; monga Yehova anamuuza Mose.