Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 38:16 - Buku Lopatulika

Nsalu zotchingira zonse za pabwalo pozungulira zinali za bafuta wa thonje losansitsa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nsalu zochingira zonse za pabwalo pozungulira zinali za bafuta wa thonje losansitsa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nsalu zonse zochinga kuzungulira bwalolo zinali za bafuta wosalala ndi wopikidwa bwino.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Katani yonse yotchinga kuzungulira chihema inali yofewa, yosalala ndi yolukidwa bwino.

Onani mutuwo



Eksodo 38:16
2 Mawu Ofanana  

momwemonso pa mbali ina: pa mbali ino ndi pa mbali ina ya chipata cha pabwalo panali nsalu zotchingira za mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zitatu, ndi makamwa ake atatu.


Ndipo makamwa a nsichi anali amkuwa; zokowera za nsichi ndi mitanda yake zasiliva; ndi zokutira mitu yake zasiliva; ndi nsichi zonse za pabwalo zinagwirana pamodzi ndi siliva.