Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 38:13 - Buku Lopatulika

Ndi pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mikono makumi asanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi pa mbali ya kum'mawa, kum'mawa, mikono makumi asanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa mbali inayo yakuvuma panalinso mamita 23.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mbali yakummawa, kotulukira dzuwa, inalinso yotalika mamita 23.

Onani mutuwo



Eksodo 38:13
2 Mawu Ofanana  

Ndi pa mbali ya kumadzulo panali nsalu zotchingira za mikono makumi asanu, nsichi zake khumi, ndi makamwa ake khumi; zokowera za nsichi ndi mitanda yake yasiliva.


Nsalu zotchingira za pa mbali imodzi ya chipata nza mikono khumi ndi isanu; nsichi zake zitatu, ndi makamwa ake atatu;