Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 26:20 - Buku Lopatulika

ndi pa mbali yake ina ya chihema, mbali ya kumpoto, pakhale matabwa makumi awiri; ndi makamwa asiliva makumi anai;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi pa mbali yake ina ya Kachisi, mbali ya kumpoto, pakhale matabwa makumi awiri; ndi makamwa asiliva makumi anai;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo kumpoto kwa chihemacho upangenso mafulemu makumi aŵiri,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo mbali yakumpoto ya chihemacho upangenso maferemu makumi awiri.

Onani mutuwo



Eksodo 26:20
2 Mawu Ofanana  

Nuzipanga makamwa makumi anai asiliva pansi pa matabwa makumi awiri; makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi kwa mitsukwa yake iwiri, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina kwa mitsukwa yake iwiri;


makamwa awiri pansi pa thabwa limodzi, ndi makamwa awiri pansi pa thabwa lina.