Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 21:25 - Buku Lopatulika

kutentha kulipa kutentha, bala kulipa bala, mkwapulo kulipa mkwapulo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kutentha kulipa kutentha, bala kulipa bala, mkwapulo kulipa mkwapulo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

kutentha ndi moto kulipa kutentha ndi moto, bala kulipa bala, ndipo mkwingwirima kulipa mkwingwirima.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kutentha ndi moto kulipa kutentha ndi moto, bala kulipa bala, mkwingwirima kulipa mkwingwirima.

Onani mutuwo



Eksodo 21:25
4 Mawu Ofanana  

diso kulipa diso, dzino kulipa dzino, dzanja kulipa dzanja, phazi kulipa phazi,


Munthu akampanda mnyamata wake, kapena mdzakazi wake, padiso, nalithudzula, azimlola amuke waufulu chifukwa cha diso lake.


Munthu akachititsa mnansi wake chilema, monga umo anachitira momwemo amchitire iye;


Ndipo diso lanu lisachite chifundo, moyo kulipa moyo, diso kulipa diso, dzino kulipa dzino, dzanja kulipa dzanja, phazi kulipa phazi.