Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 21:23 - Buku Lopatulika

Koma ngati kupweteka kukalipo, uzipereka moyo kulipa moyo,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ngati kuphweteka kukalipo, uzipereka moyo kulipa moyo,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma maiyo akampweteka, chilango chake chidzakhala chotere: moyo kulipa moyo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma ngati wavulazidwa kwambiri, ndiye malipiro ake adzakhala motere: moyo kulipa moyo,

Onani mutuwo



Eksodo 21:23
4 Mawu Ofanana  

Munthu akachititsa mnansi wake chilema, monga umo anachitira momwemo amchitire iye;


kuthyola kulipa kuthyola, diso kulipa diso, dzino kulipa dzino; monga umo anachitira munthu chilema, momwemo amchitire iye.


Musamalandira dipo lakuombola moyo wa iye adapha munthu, napalamula imfa; koma aziphedwa ndithu.


Ndipo diso lanu lisachite chifundo, moyo kulipa moyo, diso kulipa diso, dzino kulipa dzino, dzanja kulipa dzanja, phazi kulipa phazi.