Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 19:25 - Buku Lopatulika

Pamenepo Mose anawatsikira anthu, nanena nao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Mose anawatsikira anthu, nanena nao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Mose adatsikira kwa anthu kuja kukaŵauza zimenezo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Mose anatsika ndi kukawawuza anthuwo.

Onani mutuwo



Eksodo 19:25
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anati kwa iye, Muka, tsika; nukwere iwe ndi Aroni pamodzi ndi iwe; koma ansembe ndi anthu asapyole kukwera kwa Yehova, angawapasule.


Ndipo Mulungu ananena mau onse amenewa, nati,


(ndinalinkuima pakati pa Yehova ndi inu muja, kukulalikirani mau a Yehova; popeza munachita mantha chifukwa cha moto, osakwera m'phirimo) ndi kuti: