Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 16:30 - Buku Lopatulika

Ndipo anthu anapumula tsiku lachisanu ndi chiwiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anthu anapumula tsiku lachisanu ndi chiwiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero anthu sankagwira ntchito pa tsiku lachisanu ndi chiŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kotero anthu anapuma tsiku lachisanu ndi chiwiri.

Onani mutuwo



Eksodo 16:30
5 Mawu Ofanana  

Taonani, popeza Yehova anakupatsani Sabata, chifukwa chake tsiku lachisanu ndi chimodzi alikupatsa inu mkate wofikira masiku awiri; khalani yense m'malo mwake munthu asatuluke m'malo mwake tsiku lachisanu ndi chiwiri.


Ndipo mbumba ya Israele inautcha dzina lake Mana; ndiwo ngati zipatso zampasa, oyera; powalawa akunga timitanda tosakaniza ndi uchi.


Masiku asanu ndi limodzi azigwira ntchito; koma lachisanu ndi chiwiri ndilo Sabata lakupumula, msonkhano wopatulika; musamagwira ntchito konse; ndilo Sabata la Yehova m'nyumba zanu zonse.


Momwemo utsalira mpumulo wa Sabata wa kwa anthu a Mulungu.