Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 6:21 - Buku Lopatulika

Pamenepo Daniele anati kwa mfumu, Mfumu, mukhale ndi moyo chikhalire.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Daniele anati kwa mfumu, Mfumu, mukhale ndi moyo chikhalire.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Danieli anayankha kuti, “Inu mfumu mukhale ndi moyo wautali!

Onani mutuwo



Danieli 6:21
5 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinati kwa mfumu, Mfumu ikhale ndi moyo kosatha; ilekerenji nkhope yanga kuchita chisoni, popeza pali bwinja kumzinda kuli manda a makolo anga, ndi zipata zake zopsereza ndi moto.


Pamenepo Ababiloni anati kwa mfumu mu Chiaramu, Mfumu, mukhale ndi moyo chikhalire: mufotokozere anyamata anu lotoli, ndipo tidzakuuzani kumasulira kwake.


Pamenepo Nebukadinezara anayandikira pa khomo la ng'anjo yotentha yamoto, analankhula, nati, Sadrake, Mesaki, ndi Abedenego, inu atumiki a Mulungu Wam'mwambamwamba, tulukani, idzani kuno. Pamenepo Sadrake, Mesake, ndi Abedenego, anatuluka m'kati mwa moto.


Anayankha, nati kwa mfumu Nebukadinezara, Mfumu, mukhale ndi moyo chikhalire.


Ndipo akulu awa ndi akalonga anasonkhana kwa mfumu mofulumira, natero nayo, Mfumu Dariusi, mukhale ndi moyo chikhalire.