Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 5:24 - Buku Lopatulika

Pamenepo nsonga ya dzanja inatumidwa kuchokera pamaso pake, nililembedwa lembali.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo nsonga ya dzanja inatumidwa kuchokera pamaso pake, nililembedwa lembali.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Iye watumiza dzanja limene lalemba mawu amenewa.

Onani mutuwo



Danieli 5:24
2 Mawu Ofanana  

Ndipo lemba lolembedwa ndi ili: MENE MENE TEKEL ndi PARSIN.


Nthawi yomweyo zinabuka zala za dzanja la munthu, ndipo zinalemba pandunji pa choikaponyali, pomata pa khoma la chinyumba cha mfumu; ndipo mfumu inaona nsonga yake ya dzanja lidalembalo.