Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 2:33 - Buku Lopatulika

miyendo yake yachitsulo, mapazi ake mwina chitsulo mwina dongo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

miyendo yake yachitsulo, mapazi ake mwina chitsulo mwina dongo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Miyendo yake inali yachitsulo, mapazi ake anali achitsulo chosakaniza ndi dongo.

Onani mutuwo



Danieli 2:33
5 Mawu Ofanana  

Fano ili tsono, mutu wake unali wagolide wabwino, chifuwa chake ndi manja ake zasiliva, mimba yake ndi chuuno chake zamkuwa,


Munali chipenyere kufikira mwala unasemedwa popanda manja, umene unagunda fanoli pa mapazi ake okhala chitsulo ndi dongo, nuwaphwanya.