Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Aefeso 2:9 - Buku Lopatulika

chosachokera kuntchito, kuti asadzitamandire munthu aliyense.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

chosachokera kuntchito, kuti asadzitamandire munthu aliyense.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Munthu sapulumuka chifukwa cha ntchito zake, kuwopa kuti angamanyade.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

osati ndi ntchito, kuti wina aliyense asadzitamandire.

Onani mutuwo



Aefeso 2:9
9 Mawu Ofanana  

Koma ngati kuli ndi chisomo, sikulinso ndi ntchito ai; ndipo pakapanda kutero, chisomo sichikhalanso chisomo.


chifukwa kuti pamaso pake palibe munthu adzayesedwa wolungama ndi ntchito za lamulo; pakuti uchimo udziwika ndi lamulo.


Pakuti ngati Abrahamu anayesedwa wolungama chifukwa cha ntchito, iye akhala nacho chodzitamandira; koma kulinga kwa Mulungu ai.


pakuti anawo asanabadwe, kapena asanachite kanthu kabwino kapena koipa, kuti kutsimikiza mtima kwa Mulungu monga mwa kusankha kukhale, si chifukwa cha ntchito ai, koma chifukwa cha wakuitanayo,


Chotero sichifuma kwa munthu amene afuna, kapena kwa iye amene athamanga, koma kwa Mulungu amene achitira chifundo.


amene anatipulumutsa ife, natiitana ife ndi maitanidwe oyera, si monga mwa ntchito zathu, komatu monga mwa chitsimikizo mtima cha Iye yekha, ndi chisomo, chopatsika kwa ife mwa Khristu Yesu nthawi zisanayambe,