Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 11:18 - Buku Lopatulika

Pamenepo Yowabu anatumiza munthu nauza Davide zonse za nkhondoyi;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo Yowabu anatumiza munthu nauza Davide zonse za nkhondoyi;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zitatero, Yowabu adatuma wamthenga kwa Davide kukamuuza zonse zimene zidachitika kunkhondoko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yowabu anatumiza wamthenga kwa Davide kukafotokoza mwatsatanetsatane za nkhondoyo.

Onani mutuwo



2 Samueli 11:18
3 Mawu Ofanana  

Ndipo akumzindawo anatuluka, namenyana ndi Yowabu; ndipo adagwapo anthu ena, ndiwo a anyamata a Davide; ndi Uriya Muhiti anafanso.


nauza mthengawo kuti, Utatsiriza kuuza mfumu zonse za nkhondozo;


Nudza mthenga, numfotokozera, kuti, Abwera nayo mitu ya ana a mfumu. Nati iye, Muiunjike miulu iwiri polowera pa chipata kufikira m'mawa.