Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 5:2 - Buku Lopatulika

Pakutinso m'menemo tibuula, ndi kukhumbitsa kuvekedwa ndi chokhalamo chathu chochokera Kumwamba;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakutinso m'menemo tibuula, ndi kukhumbitsa kuvekedwa ndi chokhalamo chathu chochokera Kumwamba;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nchifukwa chake tsono tikubuula ndi kulakalaka kuvala nyumba yathu yakumwambayo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakali pano tibuwula, ndi kulakalaka kuvala nyumba yathu ya kumwambayo,

Onani mutuwo



2 Akorinto 5:2
8 Mawu Ofanana  

Munandiveka khungu ndi mnofu, ndi kundilumikiza mafupa ndi mitsempha.


Munthu wosauka ine; adzandilanditsa ndani m'thupi la imfa iyi?


Ndipo si chotero chokha, koma ife tomwe, tili nazo zipatso zoyamba za Mzimu, inde ifenso tibuula m'kati mwathu, ndi kulindirira umwana wathu, ndiwo chiomboledwe cha thupi lathu.


Taonani, ndikuuzani chinsinsi; sitidzagona tonse, koma tonse tidzasandulika,


Koma ndipanidwa nazo ziwirizi, pokhala nacho cholakalaka cha kuchoka kukhala ndi Khristu, ndiko kwabwino koposaposatu;