Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 13:6 - Buku Lopatulika

Koma ndiyembekeza kuti mudzazindikira kuti sitili osatsimikizidwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ndiyembekeza kuti mudzazindikira kuti sitili osatsimikizidwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma ndikhulupirira kuti mudzazindikira kuti ife sitidalephere.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo ndikhulupirira kuti mudzazindikira kuti ife sitinalephere mayesowo.

Onani mutuwo



2 Akorinto 13:6
6 Mawu Ofanana  

Ndipo monga iwo anakana kukhala naye Mulungu m'chidziwitso chao, anawapereka Mulungu kumtima wokanika, kukachita zinthu zosayenera;


Pakuti ndiopa, kuti kaya, pakudza ine, sindidzakupezani inu otere onga ndifuna, ndipo ine ndidzapezedwa ndi inu wotere wonga simufuna; kuti kaya pangakhale chotetana, kaduka, mikwiyo, zilekanitso, maugogodi, ukazitape, zodzikuza, mapokoso;


Chifukwa cha ichi ndilembera izi pokhala palibe ine, kuti pokhala ndili pomwepo ndingachite mowawitsa, monga mwa ulamuliro umene Ambuye anandipatsa ine wakumangirira, ndipo si wakugwetsa.


Dziyeseni nokha, ngati muli m'chikhulupiriro, dzitsimikizeni nokha. Kapena simuzindikira kodi za inu nokha kuti Yesu Khristu ali mwa inu? Mukapanda kukhala osatsimikizidwa.


Ndipo tipemphera Mulungu kuti musachite kanthu koipa; sikuti ife tikaoneke ovomerezeka, koma kuti inu mukachite chabwino, tingakhale ife tikhala monga osatsimikizidwa.