Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 10:9 - Buku Lopatulika

kuti ndisaoneke monga ngati kukuopsani mwa makalatawo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kuti ndisaoneke monga ngati kukuopsani mwa akalatawo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono musayese kuti ndikungokuwopsezani ndi makalata anga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine sindikufuna kuoneka ngati ndikukuopsezani ndi makalata anga.

Onani mutuwo



2 Akorinto 10:9
4 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake musaweruze kanthu isanadze nthawi yake, kufikira akadze Ambuye, amenenso adzaonetsera zobisika za mdima, nadzasonyeza zitsimikizo za mtima; ndipo pamenepo yense adzakhala nao uyamiko wake wa kwa Mulungu.


Pakuti, makalatatu, ati, ndiwo olemera, ndi amphamvu; koma maonekedwe a thupi lake ngofooka, ndi mau ake ngachabe.


Pakuti ndingakhale ndikadzitamandira kanthu kochulukira za ulamuliro (umene anatipatsa Ambuye kukumangirira, ndipo si kukugwetsera kwanu), sindidzanyazitsidwa;