Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 8:16 - Buku Lopatulika

Ndipo idzatenga akapolo anu, ndi adzakazi anu, ndi anyamata anu okongola koposa, ndi abulu anu, nidzawagwiritsa ntchito yake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo idzatenga akapolo anu, ndi adzakazi anu, ndi anyamata anu okongola koposa, ndi abulu anu, nidzawagwiritsa ntchito yake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Idzakulandani antchito anu aamuna ndi adzakazi anu. Idzakulandaninso ng'ombe zanu zonenepa ndi abulu anu, ndi kumazigwiritsa ntchito zake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mfumuyo idzatenga antchito anu aamuna ndi aakazi. Idzatenganso ngʼombe zanu zabwino ndi abulu anu nʼkumazingwiritsa ntchito.

Onani mutuwo



1 Samueli 8:16
4 Mawu Ofanana  

Taonani, ndi machira a Solomoni; pazingapo amuna amphamvu makumi asanu ndi limodzi, a mwa ngwazi za Israele.


Koma kapolo uyo akanena mumtima mwake, Mbuye wanga azengereza kudza; ndimo akayamba kupanda anyamata ndi adzakazi ndi kudya ndi kumwa, ndi kuledzera;


Ndipo idzatenga limodzi la magawo khumi la mbeu zanu, ndi la minda yanu yampesa, nidzalipatsa akapitao ake, ndi anyamata ake.


Idzatenga limodzi la magawo khumi la zoweta zanu; ndipo inu mudzakhala akapolo ake.