Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 13:20 - Buku Lopatulika

koma Aisraele onse ankatsikira kwa Afilisti, kuti awasanjire munthu yense chikhasu chake, cholimira chake, nkhwangwa yake, ndi chisenga chake;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma Aisraele onse ankatsikira kwa Afilisti, kuti awasanjire munthu yense chikhasu chake, cholimira chake, nkhwangwa yake, ndi chisenga chake;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero Mwisraele aliyense ankapita kwa Afilisti kukasanjitsa pulao kapena khasu lake, ndi kukanoletsa nkhwangwa yake kapena chikwakwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kotero Aisraeli onse amapita kwa Afilisti kukanoletsa mapulawo, makasu, nkhwangwa ndi zikwakwa zawo.

Onani mutuwo



1 Samueli 13:20
5 Mawu Ofanana  

Nateronso m'mizinda ya Manase, ndi Efuremu, ndi Simeoni, mpaka Nafutali, m'mabwinja mwao mozungulira.


Chitsulo chinola chitsulo; chomwecho munthu anola nkhope ya mnzake.


ndikanola lupanga langa lonyezimira, ndi dzanja langa likagwira chiweruzo; ndidzabwezera chilango ondiukira, ndi kulanga ondida.


Ndipo m'dziko lonse la Israele simunapezeke wosula; popeza Afilisti adati, Kuti Aisraele angadzisulire malupanga kapena mikondo;


ndipo mtengo wakukonza makasu, ndi zikhasu ndi makasu a mano unali masekeli awiri mwa atatu ndi mtengo wa nkhwangwazo; ndi kusongola zotwikira unali sekeli imodzi mwa atatu.