Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 10:15 - Buku Lopatulika

Ndipo mbale wa atate wa Saulo anati, Undiuze chimene Samuele analankhula nawe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mbale wa atate wa Saulo anati, Undiuze chimene Samuele analankhula nawe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo mbale wa bambo wakeyo adati, “Ndikukupempha, uzeko zimene adanena Samuele.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amalume ake a Sauli anati, “Chonde, ndifotokozereniko zimene Samueli wakuwuzani.”

Onani mutuwo



1 Samueli 10:15
3 Mawu Ofanana  

Ndipo akulu onse anadza kwa Yeremiya, namfunsa; ndipo iye ananena nao monga mwa mau onsewo anamuuza mfumu. Ndipo analeka kunena naye; pakuti sikunamveke mlandu.


Ndipo mbale wa atate wake wa Saulo ananena kwa iye ndi mnyamata wake, Munanka kuti? Ndipo iye anati, Kukafuna abuluwo; ndipo pakuona kuti sitinawapeze, tinadza kwa Samuele.


Ndipo Saulo anati kwa mbale wa atate wake, Anatiuza momveka kuti abuluwo anapezedwa kale. Koma sanamdziwitse mau aja Samuele ananena za ufumuwo.