Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 10:13 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene adatha kunenera anafika kumsanjeko.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene adatha kunenera anafika kumsanjeko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atatha kulosako, Saulo adapita ku kachisi ku phiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Sauli atasiya kuloserako, anapita ku kachisi ku phiri.

Onani mutuwo



1 Samueli 10:13
2 Mawu Ofanana  

Ndipo munthu wina wa komweko anayankha nati, Ndipo atate wao ndiye yani? Chifukwa chake mauwa anakhala ngati mwambi, Kodi Saulonso ali mwa aneneri?


Ndipo mbale wa atate wake wa Saulo ananena kwa iye ndi mnyamata wake, Munanka kuti? Ndipo iye anati, Kukafuna abuluwo; ndipo pakuona kuti sitinawapeze, tinadza kwa Samuele.