Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yuda 1:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Chifundo, mtendere ndi chikondi zikhale nanu mochuluka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

2 Chifundo ndi mtendere ndi chikondi zikuchulukireni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Chifundo ndi mtendere ndi chikondi zikuchulukireni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Mulungu achulukitse chifundo chake, mtendere wake ndi chikondi chake kwa inu.

Onani mutuwo Koperani




Yuda 1:2
6 Mawu Ofanana  

Ndikulembera kwa onse okhala ku Roma amene Mulungu amakukondani nakuyitanani kuti mukhale oyera mtima. Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi kwa Ambuye Yesu Khristu zikhale ndi inu.


Mtendere ndi chifundo zikhale kwa onse amene amatsata chiphunzitso ichi, ndi pa Israeli wa Mulungu.


Kwa Timoteyo mwana wanga weniweni mʼchikhulupiriro. Chisomo, chifundo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi Khristu Yesu Ambuye athu zikhale ndi iwe.


Mulungu Atate anakusankhani, atakudziwani kuyambira pachiyambi, ndipo Mzimu Woyera wakuyeretsani kuti mumvere Yesu Khristu ndikutsukidwa ndi magazi ake. Chisomo ndi mtendere zikhale ndi inu mochuluka.


Chisomo ndi mtendere zochuluka zikhale nanu pomudziwa Mulungu ndi Yesu Ambuye athu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa