Yohane 4:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iye anachoka ku Yudeya ndi kubwereranso ku Galileya. Onani mutuwoBuku Lopatulika3 anachokera ku Yudeya, namukanso ku Galileya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 anachokera ku Yudeya, namukanso ku Galileya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pamene Yesu adadziŵa kuti Afarisi azimva zimenezi, adachokako ku Yudeya napitanso ku Galileya. Onani mutuwo |