Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 4:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Iye anachoka ku Yudeya ndi kubwereranso ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 anachokera ku Yudeya, namukanso ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 anachokera ku Yudeya, namukanso ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Pamene Yesu adadziŵa kuti Afarisi azimva zimenezi, adachokako ku Yudeya napitanso ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:3
11 Mawu Ofanana  

Pamene akuzunzani pamalo ena thawirani kwina. Pakuti ndikuwuzani zoonadi kuti simudzamaliza mizinda yonse ya Israeli Mwana wa Munthu asanabwere.


Yesu anachoka pamodzi ndi ophunzira ake napita ku nyanja, ndipo gulu lalikulu la anthu lochokera ku Galileya linamutsata.


Tsopano Yesu anayenda mʼmalire a pakati pa Samariya ndi Galileya pa ulendo wake wa ku Yerusalemu.


Pa tsiku lotsatira Yesu anaganiza zopita ku Galileya. Atamupeza Filipo, anati kwa iye, “Nditsate.”


Kenaka Yesu anabwereranso kutsidya la mtsinje wa Yorodani kumalo kumene Yohane ankabatiza mʼmasiku akale. Iye anakhala kumeneko


Chifukwa cha ichi Yesu sanayendenso moonekera pakati pa Ayuda. Mʼmalo mwake Iye anapita ku chigawo cha kufupi ndi chipululu, ku mudzi wa Efereimu, kumene Iye anakhalako ndi ophunzira ake.


Ichi chinali chizindikiro chodabwitsa choyamba chimene Yesu anachita ku Kana wa ku Galileya. Potero Iye anawulula ulemerero wake, ndipo ophunzira ake anamukhulupirira Iye.


Zitatha izi, Yesu ndi ophunzira ake anapita mʼmadera a ku midzi ya ku Yudeya, kumene Iye anakhala kanthawi akubatiza.


Iye achita umboni pa zimene waziona ndi kuzimva, koma palibe avomereza umboni wake.


Munthu uyu atamva kuti Yesu wafika ku Galileya kuchokera ku Yudeya, anapita kwa Iye, namupempha kuti apite akachiritse mwana wakeyo, amene anali pafupi kufa.


Zitatha izi Yesu anayendayenda mu Galileya, ndi cholinga chakuti asafike ku Yudeya chifukwa Ayuda kumeneko amadikira kuti amuphe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa