Yohane 16:2 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iwo adzakuchotsani mʼsunagoge mwawo. Kunena zoona, nthawi ikubwera imene aliyense amene adzakuphani adzaganiza kuti akutumikira Mulungu. Onani mutuwoBuku Lopatulika2 Adzakutulutsani m'masunagoge, koma ikudza nthawi imene yense wakupha inu adzayesa kuti atumikira Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Adzakutulutsani m'masunagoge, koma ikudza nthawi imene yense wakupha inu adzayesa kuti atumikira Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adzakudulani ku mpingo. Komanso nthaŵi ilikudza yakuti aliyense amene adzakuphani, adzayesa kuti akutumikira Mulungu. Onani mutuwo |