Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Obadiya 1:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Koma Esau adzalandidwa zinthu zonse, chuma chake chobisika chidzabedwa!

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 Ha! Za Esau zasanthulidwa; ha! Zobisika zake zafunidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ha! Za Esau zasanthulidwa; ha! Zobisika zake zafunidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Onani m'mene alisakazira dziko la Esau, ndi m'mene achifunkhira chuma chake chonse.

Onani mutuwo Koperani




Obadiya 1:6
8 Mawu Ofanana  

Inu Yehova, mwandisanthula ndipo mukundidziwa.


Ana awo akhanda adzaphwanyidwa iwo akuona; nyumba zawo zidzafunkhidwa ndipo akazi awo adzagwiriridwa.


Ndidzakupatsa chuma chobisika mu mdima, katundu wa pamalo obisika, kotero kuti udziwe kuti Ine ndine Yehova Mulungu wa Israeli, amene ndakuyitana pokutchula dzina.


Koma ine ndazivula zidzukulu za Esau. Ndaonetsa poyera malo awo obisalamo, kotero kuti sadzathanso kubisala. Ana ake, abale ake pamodzi ndi anansi ake awonongeka. Palibe wonena kuti,


Imfa ilunjike pa akavalo ake ndi magaleta ake. Ilunjikanso pa magulu ankhondo achilendo amene ali pakati pawo kuti asanduke ngati akazi. Chiwonongeko chilunjikenso pa chuma chake kuti chidzafunkhidwe.


Amavumbulutsa zinthu zozama ndi zobisika; amadziwa zimene zili mu mdima, ndipo kuwunika kumakhala ndi Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa