Obadiya 1:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma Esau adzalandidwa zinthu zonse, chuma chake chobisika chidzabedwa! Onani mutuwoBuku Lopatulika6 Ha! Za Esau zasanthulidwa; ha! Zobisika zake zafunidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ha! Za Esau zasanthulidwa; ha! Zobisika zake zafunidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Onani m'mene alisakazira dziko la Esau, ndi m'mene achifunkhira chuma chake chonse. Onani mutuwo |