Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 8:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 “Tenga Alevi pakati pa Aisraeli ndipo uwayeretse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 Uwatenge Alevi pakati pa ana a Israele, nuwayeretse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Uwatenge Alevi pakati pa ana a Israele, nuwayeretse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 “Upatule Alevi pakati pa Aisraele, ndipo uŵayeretse.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 8:6
10 Mawu Ofanana  

Ana anga, musanyalanyaze tsopano, pakuti Yehova wakusankhani kuti muziyima pamaso pake ndi kumutumikira Iye, kugwira ntchito pamaso pake ndi kufukiza lubani.”


Kenaka iye anati kwa anthu, “Konzekerani tsiku lachitatu, musagone pamodzi ndi mkazi.”


Nyamukani, nyamukani, chokaniko ku Babuloniko! Musakhudze kanthu kodetsedwa! Inu amene mumanyamula ziwiya za Yehova tulukanimo ndipo mudziyeretse.


Wansembe amene ati ayeretse munthu wodwalayo amuyimitse munthuyo ali ndi zopereka zake zonse pamaso pa Yehova pa khomo la tenti ya msonkhano.


Iye adzachita kukhalira pansi ngati mmisiri woyenga ndi woyeretsa siliva. Iye adzayeretsa Alevi ndi kuwayenga ngati golide ndi siliva. Pamenepo Yehova adzakhala ndi anthu amene azidzabweretsa zopereka mwachilungamo,


“Bweretsa fuko la Levi ndipo ulipereke kwa Aaroni wansembe kuti lizimutumikira.


Yehova anawuza Mose kuti,


Abwenzi okondedwa, popeza tili ndi malonjezo amenewa, tiyeni tidziyeretse, kusiyana nazo zilizonse zimene zikhoza kudetsa thupi ndi mzimu, ndipo tiyesetse kukhala oyera mtima poopa Mulungu.


Pa nthawi imeneyo Yehova anapatula fuko la Levi kuti anyamule bokosi la pangano la Yehova lija, kuti ayimirire pamaso pa Yehova, kutumikira ndi kunena madalitso pa dzina lake monga amachitira mpaka lero.


Sendezani kufupi ndi Mulungu ndipo Iye adzasendeza kwa inu. Sambani mʼmanja mwanu, inu anthu ochimwa. Yeretsani mitima yanu, inu anthu okayikira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa