Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 8:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

5 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 8:5
4 Mawu Ofanana  

Abale awo Alevi anapatsidwa ntchito zina zonse ku malo opatulika ku nyumba ya Mulungu.


Choyikapo nyalecho chinapangidwa motere: chinasulidwa kuchokera ku golide, kuyambira pa tsinde pake mpaka ku maluwa ake. Choyikapo nyalecho chinapangidwa monga momwe Yehova anaonetsera Mose.


“Tenga Alevi pakati pa Aisraeli ndipo uwayeretse.


Pa nthawi imeneyo Yehova anapatula fuko la Levi kuti anyamule bokosi la pangano la Yehova lija, kuti ayimirire pamaso pa Yehova, kutumikira ndi kunena madalitso pa dzina lake monga amachitira mpaka lero.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa