Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 8:10 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ubwere nawo pamaso pa Yehova, ndipo Aisraeli asanjike manja awo pa iwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

10 nubwere nao Alevi pamaso pa Yehova; ndi ana a Israele aike manja ao pa Alevi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 nubwere nao Alevi pamaso pa Yehova; ndi ana a Israele aike manja ao pa Alevi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Pamene ukuŵapereka Aleviwo pamaso pa Chauta, Aisraele asanjike manja ao pa Alevi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 8:10
7 Mawu Ofanana  

Munthuyo asanjike dzanja lake pa mutu pa nsembe yopserezayo, ndipo idzalandiridwa kuti ikhale yopepesera machimo ake.


Akuluakulu a anthuwo asanjike manja awo pa mutu pa ngʼombe pamaso pa Yehova, ndipo ayiphe pomwepo pamaso pa Yehova.


“Tenga Alevi mʼmalo mwa ana aamuna oyamba kubadwa onse a Aisraeli, ndiponso zoweta zonse za Alevi mʼmalo mwa zoweta za Aisraeli. Alevi ndi anga. Ine ndine Yehova.


Iwo anapereka anthuwa kwa atumwi amene anawapempherera ndi kuwasanjika manja.


Usanyozere mphatso yako yomwe inapatsidwa kwa iwe kudzera mʼmawu auneneri pamene gulu la akulu ampingo linakusanjika manja.


Usafulumire kusanjika manja munthu, ndipo usavomerezane ndi anthu ena pa machimo. Usunge bwino kuyera mtima kwako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa