Numeri 7:18 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pa tsiku lachiwiri, Natanieli mwana wa Zuwara, mtsogoleri wa Isakara, anabweretsa chopereka chake. Onani mutuwoBuku Lopatulika18 Tsiku lachiwiri Netanele mwana wa Zuwara, kalonga wa Isakara, anabwera nacho chake: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Tsiku lachiwiri Netanele mwana wa Zuwara, kalonga wa Isakara, anabwera nacho chake: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Netanele mwana wa Zuwara, mtsogoleri wa fuko la Isakara, adapereka zopereka zake pa tsiku lachiŵiri. Onani mutuwo |