Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 5:13 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 nakagonana ndi mwamuna wina koma mwamuna wake wosadziwa, ndipo palibe wina aliyense wadziwa za kudzidetsa kwake (pakuti palibe mboni yomuneneza chifukwa sanagwidwe akuchita),

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

13 ndi munthu akagona naye, koma kumbisikira maso a mwamuna wake, ndi kumng'unira; nadetsedwa mkaziyo, koma palibe mboni yomtsutsa, kapena sanamgwire alimkuchita;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 ndi munthu akagona naye, koma kumbisikira maso a mwamuna wake, ndi kumng'unira; nadetsedwa mkaziyo, koma palibe mboni yomtsutsa, kapena sanamgwire alimkuchita;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Mwamuna wina atachita naye chigololo, zimenezo zitha kubisika, mwamuna wake osazidziŵa. Mkaziyo atha kukhala wosazindikirika kuti wadziipitsa, chifukwa chosoŵa mboni yomtsutsa, popeza kuti sadampezerere akuchita kumene.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 5:13
6 Mawu Ofanana  

Umu ndi mʼmene mkazi amachitira atachita chigololo: Atatha kudya ndi kupukuta pakamwa pake iye amanena kuti “Sindinachite kalikonse kolakwa.”


Anatenga thumba la ndalama ndipo adzabwera ku nyumba mwezi ukakhwima.”


Mumadalira lupanga lanu, mumachita zinthu zonyansa, ndipo aliyense wa inu amachita chigololo ndi mkazi wa mnzake. Kodi inu nʼkulandira dzikoli?’


“ ‘Usagonane ndi mkazi wa mnzako ndi kudziyipitsa naye.


“ ‘Ngati munthu wachita chigololo ndi mkazi wa mnzake, mwamunayo pamodzi ndi mkaziyo ayenera kuphedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa