Numeri 4:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ndipo azikuta bokosilo ndi zikopa za akatumbu ndi kuyala pamwamba pake nsalu ya mtundu wa thambo ndi kuyika mitengo yonyamulira mʼmalo mwake. Onani mutuwoBuku Lopatulika6 ndi kuikapo chophimba cha zikopa za akatumbu; ndi kuyalapo nsalu yamadzi yeniyeni, ndi kupisako mphiko zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndi kuikapo chophimba cha zikopa za akatumbu; ndi kuyalapo nsalu yamadzi yeniyeni, ndi kupisako mphiko zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pambuyo pake ayalepo zikopa zambuzi, ndipo pamwamba pake ayalepo nsalu yobiriŵira, ndi kupisa mphiko m'zigwinjiri zake. Onani mutuwo |