Numeri 3:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Pereka Alevi kwa Aaroni ndi kwa ana ake aamuna. Amenewa ndiwo Aisraeli amene aperekedwa kwa iye kwathunthu. Onani mutuwoBuku Lopatulika9 Ndipo uzipereka Alevi kwa Aroni ndi kwa ana ake aamuna; apatsidwa kwa iye ndithu, ochokera kwa ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo uzipereka Alevi kwa Aroni ndi kwa ana ake amuna; apatsidwa kwa iye ndithu, ochokera kwa ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Aleviwo uŵapereke kwa Aroni ndi kwa ana ake aamuna. Uŵapereke kwathunthu kwa iyeyo, kuŵachotsa pakati pa Aisraele. Onani mutuwo |