Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 3:11 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Yehova anawuzanso Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

11 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 3:11
3 Mawu Ofanana  

Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Apo mudzadziwa kuti Ine ndatumiza chenjezoli kuti pangano langa ndi Levi lipitirire.


Usankhe Aaroni ndi ana ake aamuna kuti azitumikira pa ntchito ya unsembe. Koma wina aliyense woyandikira malo opatulika aphedwe.”


“Pakati pa Aisraeli onse ndatenga Alevi kulowa mʼmalo mwa mwana wamwamuna aliyense woyamba kubadwa kwa amayi a Chiisraeli. Alevi ndi anga,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa