Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 26:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 ndipo ana a Eliabu anali Nemueli, Datani ndi Abiramu. Datani ndi Abiramu anali gulu la akuluakulu aja amene anawukira Mose ndi Aaroni ndipo analinso mʼgulu la otsatira Kora pamene anawukira Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

9 Ndi ana a Eliyabu: Nemuwele, ndi Datani ndi Abiramu. Iwo ndiwo Datani ndi Abiramu omwe aja oitanidwa a khamu, amene anatsutsana ndi Mose ndi Aroni mu msonkhano wa Kora, muja anatsutsana ndi Yehova;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndi ana a Eliyabu: Nemuwele, ndi Datani ndi Abiramu. Iwo ndiwo Datani ndi Abiramu omwe aja oitanidwa a khamu, amene anatsutsana ndi Mose ndi Aroni mu msonkhano wa Kora, muja anatsutsana ndi Yehova;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 ndipo ana a Eliyabu anali Nemuwele, Datani ndi Abiramu. Ameneŵa anali omwe aja amene adasankhidwa mu mpingo, amenenso adakangana ndi Mose ndi Aroni pogwirizana ndi Kora, pamene adatsutsana ndi Chauta.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 26:9
5 Mawu Ofanana  

Nthaka inatsekuka ndipo inameza Datani; inakwirira gulu la Abiramu.


Amenewa ndi anthu amene anasankhidwa kuchokera mʼmagulu mwawo, eni mbumba a mafuko a makolo awo. Iwowa anali atsogoleri a mafuko a Israeli.


Mwana wa Palu anali Eliabu,


Tsoka kwa iwo chifukwa anatsatira njira ya Kaini. Iwo athamangira phindu, nʼchifukwa chake anagwa mʼtchimo la Baalamu. Iwo anawonongedwa chifukwa chowukira monga anachitira Kora.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa