Numeri 24:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Monga mkango waumuna, amabisala nagona pansi, monga mkango waukazi, adzamuputa ndani? “Amene adalitsa iwe, adalitsike ndipo amene atemberera iwe, atembereredwe!” Onani mutuwoBuku Lopatulika9 Anaunthama, nagona pansi ngati mkango, ngati mkango waukazi; adzamuutsa ndani? Wodalitsika aliyense wakudalitsa iwe, wotemberereka aliyense wakutemberera iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Anauthama, nagona pansi ngati mkango, ngati mkango waukazi; adzamuutsa ndani? Wodalitsika aliyense wakudalitsa iwe, wotemberereka aliyense wakutemberera iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Adamyata, nagona pansi ngati mkango ngati mkango wamphongo kapena waukazi. Kodi amuutse ndani? Ndi wodala munthu amene aŵadalitsa, ndi wotembereredwa munthu amene aŵatemberera.” Onani mutuwo |