Numeri 24:7 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Madzi adzayenderera mʼmitsuko yake; mbewu zake zidzakhala ndi madzi ambiri. “Mfumu yake idzakhala yamphamvu kuposa Agagi; ufumu wake udzakwezedwa. Onani mutuwoBuku Lopatulika7 Madzi adzayenda natuluka m'zotungira zake, ndi mbeu zake zidzakhala ku madzi ambiri, ndi mfumu yake idzamveka koposa Agagi, ndi ufumu wake udzamveketsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Madzi adzayenda natuluka m'zotungira zake, ndi mbeu zake zidzakhala ku madzi ambiri, ndi mfumu yake idzamveka koposa Agagi, ndi ufumu wake udzamveketsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Madzi adzasefukira m'zotungira zao, ndipo mbeu zao zidzakhala ndi madzi ambiri, mfumu yao idzakhala yotchuka kupambana Agagi, ndipo ufumu wake udzakwezedwa. Onani mutuwo |
Ulamuliro ndi mtendere wake zidzakhala zopanda malire. Iye adzalamulira ufumu wake ali pa mpando waufumu wa Davide, ndipo adzawukhazikitsa ndi kuwuchirikiza mwa chiweruzo cholungama ndi pochita zachilungamo kuyambira nthawi imeneyo mpaka muyaya. Ndi mtima wake wonse, Yehova Wamphamvuzonse watsimikiza kuchita zimenezi.