Numeri 24:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 ndipo ananena uthenga wake: “Uthenga wa Balaamu mwana wa Beori, uthenga wa amene diso lake ndi lotsekuka, Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Pamenepo ananena fanizo lake, nati, Balamu mwana wa Beori anenetsa, ndi munthuyo anatsinzina maso anenetsa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamenepo ananena fanizo lake, nati, Balamu mwana wa Beori anenetsa, ndi munthuyo anatsinzina maso anenetsa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 ndipo adayamba kulankhula mau auneneri, adati, “Mau a Balamu mwana wa Beori, mau a munthu amene maso ake ndi otsekuka, Onani mutuwo |