Numeri 24:12 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Balaamu anayankha Balaki kuti, “Kodi sindinawawuze amithenga amene munawatumiza kwa ine, Onani mutuwoBuku Lopatulika12 Ndipo Balamu anati kwa Balaki, Kodi sindinauzanso amithenga anu amene munawatumiza kwa ine, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Balamu anati kwa Balaki, Kodi sindinauzanso amithenga anu amene munawatumiza kwa ine, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Balamu adafunsa Balaki kuti “Kodi amithenga anu amene mudaŵatuma kwa ine aja, sindidaŵauze kuti, Onani mutuwo |