Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 21:1 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Mfumu ya Akanaani ya ku Aradi, imene inkakhala ku Negevi, itamva kuti Aisraeli akubwera kudzera msewu wopita ku Atarimu, inachita nkhondo ndi Aisraeli nigwira ena mwa iwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

1 Pamene Mkanani, mfumu ya Aradi, wokhala kumwera, anamva kuti Israele anadzera njira ya Atarimu, anathira nkhondo pa Israele, nagwira ena akhale ansinga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Pamene Mkanani, mfumu ya Aradi, wokhala kumwera, anamva kuti Israele anadzera njira ya Atarimu, anathira nkhondo pa Israele, nagwira ena akhale ansinga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mfumu Yachikanani ya ku Aradi imene inkakhala kumwera, itamva kuti Aisraele akubwera, kudzera njira ya ku Atarimu, idathira nkhondo Aisraelewo, nigwirako ena ukapolo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 21:1
10 Mawu Ofanana  

Kenaka Abramu ananyamuka kumalowera cha ku Negevi.


Koma Aamaleki ndi Akanaani amene ankakhala ku dziko lamapirilo anatsika ndi kumenyana nawo ndipo anawakantha mʼnjira yonse mpaka ku Horima.


Mfumu ya Akanaani ya ku Aradi yomwe inkakhala ku Negevi kummwera kwa Kanaani, inamva kuti Aisraeli akubwera.


Sihoni ndi ankhondo ake atabwera kudzakumana nafe mwankhondo pa Yahazi,


mfumu ya Horima imodzi mfumu ya Aradi imodzi


Anthu a ku Ai anathamangitsa Aisraeli kuchokera pa chipata cha mzindawo mpaka ku ngwenya ndipo anapha anthu 36. Iwowa anawapha pamene ankatsika phiri. Choncho mitima ya anthu inasweka ndipo analibenso mphamvu.


Tsono zidzukulu za Hobabu, Mkeni uja, mpongozi wa Mose, zinachoka ku Yeriko mzinda wa migwalangwa pamodzi ndi anthu a fuko la Yuda mpaka ku chipululu chimene chili kummwera kwa Aradi ndi kukakhala ndi Aamaleki.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa