Numeri 20:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anakangana ndi Mose kuti, “Kunali bwino ifenso tikanangofa pamene abale athu anafa pamaso pa Yehova! Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo anthu anatsutsana ndi Mose, nanena, nati, Mwenzi titangomwalira muja abale athu anamwalira pamaso pa Yehova! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo anthu anatsutsana ndi Mose, nanena, nati, Mwenzi titangomwalira muja abale athu anamwalira pamaso pa Yehova! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Anthuwo adayamba kukangana ndi Mose, adati, “Kukadakhala bwino tikadafera pamodzi ndi abale athu aja amene adafa pamaso pa Chauta. Onani mutuwo |