Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 2:26 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 62,700.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

26 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 ndipo ankhondo ake ngokwanira 62,700.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:26
4 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Dani chinali 62,700.


Kumpoto kudzakhala msasa wa magulu a Dani pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa Adani ndi Ahiyezeri mwana wa Amisadai.


Fuko la Aseri lidzamanga pafupi ndi iwowo. Mtsogoleri wa Aaseri ndi Pagieli mwana wa Okirani.


Onse a fuko la Asuhamu amene anawerengedwa analipo 64,400.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa