Numeri 2:22 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Lotsatira lidzakhala fuko la Benjamini. Mtsogoleri wa Abenjamini ndi Abidani mwana wa Gideoni. Onani mutuwoBuku Lopatulika22 Ndi fuko la Benjamini: kalonga wa ana a Benjamini ndiye Abidani mwana wa Gideoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndi fuko la Benjamini: kalonga wa ana a Benjamini ndiye Abidani mwana wa Gideoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tsono pabwere fuko la Benjamini, limene mtsogoleri wake ndi Abidani mwana wa Gideoni, Onani mutuwo |