Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 2:19 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 40,500.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

19 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai kudza mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai kudza mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 ndipo ankhondo ake ngokwanira 40,500.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:19
4 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Efereimu chinali 40,500.


Kumadzulo kudzakhala magulu a msasa wa Efereimu pamene pali mbendera yawo. Mtsogoleri wa Aefereimuwo ndi Elisama mwana wa Amihudi.


Fuko la Manase lidzakhala pafupi ndi Efereimu. Mtsogoleri wa Amanase ndi Gamalieli mwana wa Pedazuri.


Awa ndiwo anali mafuko a Efereimu. Amene anawerengedwa analipo 32,500. Zimenezi zinali zidzukulu za Yosefe monga mwa mafuko awo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa