Numeri 17:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pa ndodo ya Levi ulembepo dzina la Aaroni, chifukwa pafunika ndodo imodzi ya mtsogoleri pa fuko lililonse. Onani mutuwoBuku Lopatulika3 Ndipo ulembe dzina la Aroni pa ndodo ya Levi; pakuti pakhale ndodo imodzi pa mkulu yense wa nyumba za makolo ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo ulembe dzina la Aroni pa ndodo ya Levi; pakuti pakhale ndodo imodzi pa mkulu yense wa nyumba za makolo ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 ndipo ulembe dzina la Aroni pa ndodo ya Levi. Pakuti payenera kukhala ndodo imodzi pa mtsogoleri aliyense wa fuko la makolo ake. Onani mutuwo |