Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 16:4 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Mose atamva izi, anagwa chafufumimba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

4 Pamene Mose anamva ichi anagwa nkhope yake pansi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Pamene Mose anamva ichi anagwa nkhope yake pansi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Mose atamva zimenezi, adagwada napemphera,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 16:4
7 Mawu Ofanana  

Pamene iwo ankapha anthu, ine ndinatsala ndekha. Tsono ndinadzigwetsa chafufumimba ndi kufuwula kuti, “Aa, Ambuye Yehova! Kodi mwawakwiyiratu anthu a ku Yerusalemu motero kuti mudzawononga kotheratu anthu onse otsala ku Israeli?”


Koma Mose ndi Aaroni anadzigwetsa pansi chafufumimba pamaso pa Aisraeli onse omwe anasonkhana pamenepo.


Koma Mose ndi Aaroni anadzigwetsa chafufumimba ndipo analira mokweza, “Chonde Mulungu, Mulungu wa mizimu ya anthu onse, kodi mudzakwiyira gulu lonse pamene munthu mmodzi yekha ndiye amene wachimwa?”


“Chokani pakati pa gulu la anthuwa kuti ndiwawononge kamodzinʼkamodzi.” Ndipo iwo anagwa pansi chafufumimba.


Ndipo iye anawuza Kora ndi anthu onse amene ankamutsatira kuti, “Yehova mawa mmawa adzasonyeza yemwe ndi wake ndiponso amene ndi woyera mtima. Munthuyo adzabwera pafupi ndi Iye. Munthu amene adzamusankheyo adzamusendeza pafupi.


Mose ndi Aaroni anachoka mu msonkhano ndi kupita pa khomo la tenti ya msonkhano, nagwa pansi chafufumimba ndipo ulemerero wa Yehova unaonekera.


Tsono Yoswa anangʼamba zovala zake nagwada nʼkuweramitsa mutu wake pansi patsogolo pa Bokosi la Yehova. Akuluakulu a Israeli nawonso anadzigwetsa pansi ndipo anakhala pomwepo mpaka madzulo atadziwaza fumbi kumutu kwawo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa