Numeri 11:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Tikukumbukira nsomba zaulere zimene tinkadya ku Igupto komanso nkhaka, mavwende, anyezi wamitundumitundu ndi adyo. Onani mutuwoBuku Lopatulika5 Tikumbukira nsomba tinazidya mu Ejipito chabe, minkhaka, ndi mavwende, ndi anyezi wa mitundu itatu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Tikumbukira nsomba tinazidya m'Ejipito chabe, minkhaka, ndi mavwende, ndi anyezi a mitundu itatu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tikukumbukira nsomba zaulere zimene tinkadya ku Ejipito, minkhaka ija, mavwende ndi anyezi wamitundu-mitundu. Onani mutuwo |