Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 10:16 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Eliabu mwana wa Heloni ndiye anali mtsogoleri wa fuko la Zebuloni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

16 Ndi gulu la fuko la ana a Zebuloni panali Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndi gulu la fuko la ana a Zebuloni panali Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Mtsogoleri wa gulu la fuko la Zebuloni anali Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:16
4 Mawu Ofanana  

Eliabu mwana wa Heloni, kuchokera ku fuko la Zebuloni,


Mtsogoleri wa gulu la fuko la Isakara anali Netanieli mwana wa Zuwara,


Kenaka anagwetsa chihema, ndipo Ageresoni ndi Amerari amene ananyamula chihemacho, ananyamuka.


Pa tsiku lachitatu, Eliabu mwana wa Heloni, mtsogoleri wa Azebuloni, anabweretsa chopereka chake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa