Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 1:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Uziya anabereka Yotamu, Yotamu anabereka Ahazi, Ahazi anabereka Hezekiya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

9 ndi Uziya anabala Yotamu; ndi Yotamu anabala Ahazi; ndi Ahazi anabala Hezekiya;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 ndi Uziya anabala Yotamu; ndi Yotamu anabala Ahazi; ndi Ahazi anabala Hezekiya;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Uziya adabereka Yotamu, Yotamu adabereka Ahazi, Ahazi adabereka Hezekiya.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 1:9
11 Mawu Ofanana  

Mʼchaka chachiwiri cha Peka mwana wa Remaliya mfumu ya Israeli, Yotamu mwana wa Uziya mfumu ya Yuda anayamba kulamulira.


Azariya anamwalira ndipo anayikidwa mʼmanda pamodzi ndi makolo ake mu Mzinda wa Davide. Ndipo Yotamu mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.


Mfumu Uziya anali ndi khate mpaka tsiku limene anamwalira. Iye amakhala mʼnyumba ya yekha ngati wakhate, ndipo samalowa mʼNyumba ya Yehova. Yotamu mwana wake ndiye amayangʼanira nyumba yaufumu ndipo ankalamulira anthu a mʼdzikomo.


Yotamu anakhala mfumu ali ndi zaka 25 ndipo analamulira mu Yerusalemu kwa zaka 16. Dzina la amayi ake linali Yerusa mwana wa Zadoki.


Hezekiya anabereka Manase, Manase anabereka Amoni, Amoni anabereka Yosiya.


Asa anabereka Yehosafati, Yehosafati anabereka Yoramu, Yoramu anabereka Uziya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa