Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Mateyu 1:3 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Yuda anabereka Perezi ndi Zara, amene amayi awo anali Tamara. Perezi anabereka Hezironi, Hezironi anabereka Aramu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

3 ndi Yuda anabala Perezi ndi Zera mwa Tamara; ndi Perezi anabala Hezironi; ndi Hezironi anabala Ramu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 ndi Yuda anabala Perezi ndi Zera mwa Tamara; ndi Perezi anabala Hezironi; ndi Hezironi anabala Ramu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Yuda adabereka Perezi ndi Zera, mwa Tamara; Perezi adabereka Hezironi, Hezironi adabereka Ramu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 1:3
13 Mawu Ofanana  

Kenaka Yuda anati kwa mpongozi wake Tamara, “Bwererani ku nyumba ya abambo anu ndi kukhala kumeneko ngati wamasiye mpaka mwana wanga Sela atakula.” Ananena izi chifukwa ankaopa kuti Sela angafenso ngati abale ake aja. Choncho Tamara anapita kukakhala ku nyumba ya abambo ake.


Yuda anamupezera mkazi mwana wake woyamba uja Eri, ndipo dzina la mkaziyo linali Tamara.


Ana aamuna a Yuda ndi awa: Eri, Onani, Sela, Perezi ndi Zera. Koma Eri ndi Onani anamwalira mʼdziko la Kanaani. Ana a Perezi anali Hezironi ndi Hamuli.


Ana a Yuda anali awa: Perezi, Hezironi, Karimi, Huri ndi Sobali.


A banja la Zera: Yeueli. Anthu ochokera ku Yuda analipo 690.


Abrahamu anabereka Isake, Isake anabereka Yakobo, Yakobo anabereka Yuda ndi abale ake.


Aramu anabereka Aminadabu, Aminadabu anabereka Naasoni, Naasoni anabereka Salimoni.


mwana wa Aminadabu, mwana wa Arni, mwana wa Hezronu, mwana wa Perezi, mwana wa Yuda,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa