Genesis 7:8 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Nyama zoti nʼkudya ndi nyama zosadyedwa, mbalame, pamodzi ndi nyama zokwawa zonse zinadza kwa Nowa ziwiriziwiri ndi kulowa mʼchombomo. Onani mutuwoBuku Lopatulika8 Nyama zodyedwa ndi nyama zosadyedwa, ndi mbalame, ndi zonse zokwawa pansi, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Nyama zodyedwa ndi nyama zosadyedwa, ndi mbalame, ndi zonse zokwawa pansi, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Nyama zazimuna ndi zazikazi zimene anthu amaperekera nsembe, mbalame pamodzi ndi nyama zokwaŵa zomwe, Onani mutuwo |