Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Genesis 7:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ndipo Nowa anachita zonse zimene Yehova anamulamulira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

5 Ndipo anachita Nowa monga mwa zonse anamlamulira iye Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo anachita Nowa monga mwa zonse anamlamulira iye Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ndipo Nowa adachita zonse zimene Mulungu adamlamula.

Onani mutuwo Koperani




Genesis 7:5
14 Mawu Ofanana  

Nowa anachita zonse monga Mulungu anamulamulira.


Iye analowa nazo zazimuna ndi zazikazi monga mmene Mulungu anamulamulira. Kenaka Yehova anatseka pa khomo.


Pamenepo ine sindikanachititsidwa manyazi, poganizira malamulo anu onse.


Tsopano ntchito yonse ya tenti ya msonkhano inatha. Aisraeli anachita zonse monga momwe Yehova analamulira Mose.


Mose anachita zonse monga Yehova anamulamulira.


Mose ndi Aaroni anachita monga momwe Yehova anawalamulira.


Yesu anayankha kuti, “Zibatero tsopano, ndi koyenera kwa ife kuchita zimenezi kukwaniritsa chilungamo chonse.” Ndipo Yohane anavomera.


Yesu anayankha kuti, “Amayi ndi abale anga ndi amene amamva mawu a Mulungu ndi kumachita zimene mawuwo akunena.”


Ngati inu mudziwa zinthu zimenezi, mudzakhala odala mukamazichita.


Amayi ake anati kwa antchito, “Inu muchite chilichonse chimene akuwuzeni.”


Ndipo pokhala munthu choncho anadzichepetsa yekha ndipo anamvera mpaka imfa yake, imfa yake ya pamtanda!


Ngakhale Iye anali Mwana wa Mulungu anaphunzira kumvera pomva zowawa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa